12/03/2026
Anthu okonda Dancehall sakuvetsa ndipo Mafuso achuluka 👇
Kuyambira tsiku lomwe (Lawi adakamba zoti akupanga Battle ya pa stage Malinga Mafia anapephedwa kuti akapange nawo ndipo anavomeleza kuti akapezekako kuti akakutumule ana onse a hip hip-hop akawawonetsa kuti iweyo nde Fadda wa dzamba dzonse pa Malawi pano.
Koma chifukwa choti anthu anamupepha Lawi kuti ngati Malinga akapezeke kumaloko akuyenera kuti amuitanire oyimba a Dancehall anzake akamenye nawo Battle osati a Hip-hop ndipo zikuveka kuti Lawi atasikhasika wasakha Reggae and Dancehall PRESIDENT yemwe amatchedwa kuti (BLAST IMVAI) kuti akabandulane ndi Malinga pa stage
Koma Malinga atangonva phekesela yoti akabandulana ndi (Blasto Imva) osati IKK monga m'mene amaganizila Malinga Mafia wasitha maganizo ake ndipo wanenetsa kuti sakapezekaso kumaloko zimene zikuaonyeza kuti Malinga akumuopa (Blasto Imva)?
Koma Mafuso ochuluka ngati awa nde anthu akufusabe pa Social Media 👇
Kodi mesa Malinga amadzitama kuti iyeyo nde TATE wa Dancehall yaku Malawi, zomwe zimatathauza kuti palibe yemwe angamugwetse nde zitheka bwanji kuti chokha chongonva kuti dzina la Dancehall President (Blasto Imva lilipam'ndandanda wokamenya Battle iye ndikusitha maganizo kuti sakapezekokaso
Tidziti Malinga akumuopa Blasto kuti atha kukamuonongera mbiri?
Zimenezi ndizina mwa zomwe akufusana anthu okonda Dancehall komanso omwe amamutsata (Malinga komanso Dancehall President Blasto Imva) 🧔👲🧑🧑🧔
Ena akuwona ngati kuti mwina chifukwa choti Blasto wakhala akumudya Malinga m'ma Collaborations onse omwe akhala akumuna, Ndizomwe zampangitsa kuti Malinga akhale ndi matha.
Malinga amayesa kuti akaphana ndi IKK Mwatsoka wanva kuti akaphana ndi Chilombo Blasto Imva pompo wasitha maganizo kuti sapanga nawonso za Battle. 🙏