πšπšŽπšŠπš• π™³πš’πšŒπš”πš’πšŽπš£ π™Όπš 

  • Home
  • Malawi
  • Lilongwe Area 12
  • πšπšŽπšŠπš• π™³πš’πšŒπš”πš’πšŽπš£ π™Όπš 

πšπšŽπšŠπš• π™³πš’πšŒπš”πš’πšŽπš£ π™Όπš  Time to invest

uthenga sulemera
31/10/2025

uthenga sulemera

27/10/2025

πŸ—“οΈ 27 Oct 2025
Kadzutsa wa Mau; ULENDO OWERENGA BIBLE

πŸ“š Yoswa 7:1-26

*Lingaliro*
Mavuto samatha ndi kulira! Kugonja ndi "mwayi" odzifufuza ndi kukonza chomwe chalakwika. Kulephera kutero ndi tsoka; minyama yeniyeni.

πŸ“–πŸ‘€ _palemba_
19. Ndipo Yoswa anati kwa Akani, Mwana wanga, uchitiretu ulemu Yehova Mulungu wa Israyeli, numlemekeze Iye; nundiuze tsopano, wachitanji? usandibisire.

20. Ndipo Akani anayankha...

21. pamene ndinaona pazofunkha maraya abwino a ku Babulo, ndi masekeli mazana awiri a siliva, ndi chikute chagolidi, kulemera kwake masekeli makumi asanu, ndinazikhumbira ndi kuzitenga; ndipo taonani, ndazibisa m'nthaka pakati pa hema wanga, ndi siliva pansi pakepo.

Nkhani ya Akani ili ndi maphunziro ozama. Nawa ena mwa iwo:

1. Mulungu amalora anthu osachimwa afe "kunkhondo" ndipo ochimwa apulumuke, powapatsa mwayi olapa tchimo lao. Akani wakubayo anapulumuka, pomwe ankhondo 36 anafa!

2. Tchimo limaumitsa mtima kuti munthu asamve chidzudzulo. "Tilipo ambiri," amadzilimbitsa mtima, osadziwa chiweruzo ndi cha aliyense payekha. "Mudzipatule..." koma Akani sanatero; sanadziwe kuti mwayi wake unali ukutha pang'ono-pang'ono.

3. Kusekerera tchimo, m'malo modzudzula, kumasandutsa anthu kukhala othandizira tchimo (accomplices) ndipo amayenera kugawana nao zotsatira za tchimolo. Apabanja la Akani ankadziwa za katundu yemwe anabayo chotero anafa naye pamodzi.

4. Tchimo limasowetsa mtendere. Akani anafa "atabisa chuma" m'malo mochidyerera!

_"Ndipo Yoswa anati, Watisautsiranji? Yehova adzakusautsa lero lino. Ndipo, Aisrayeli onse anamponya miyala, nawatentha ndi moto..." (v 25)_

Tsoka la Akani litipatse ife lero nzeru. Amen

Who can solve this correctly
22/08/2025

Who can solve this correctly

31/07/2025
26/07/2025

*A doctor can save your body. A fireman can save your house. But only God can save your soul. Amen if you believe.β€οΈπŸ™*

"Whether a stone falls on an egg or an egg falls on a stone. The results will still be the same β€œWho can tell the meanin...
15/07/2025

"Whether a stone falls on an egg or an egg falls on a stone. The results will still be the same β€œ

Who can tell the meaning ?

GOODMORNING β˜€οΈ

( Tanthauzo logwila mtima liyikidwa madzulowa )

Kwamuthu ,osamudziwa uzingot chairman yu wazizidwa
27/05/2025

Kwamuthu ,osamudziwa uzingot chairman yu wazizidwa

14/03/2025

Zobera ayi, Talemba "Facebook" utatseka maso.

Ine : fakciboik πŸ˜‚πŸ˜‚πŸ˜‚

Address

Lilongwe Area 12

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when πšπšŽπšŠπš• π™³πš’πšŒπš”πš’πšŽπš£ π™Όπš  posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share

Category