19/08/2024
Lero ndifuna nding'alure wokwiya akwiye koma amve ndithu:
* Ngati mkadzi wanu akupanga zinthu 5 izi ndiye kuti siwanu ndipo ngati Pali mpata msiyeni palibe vuto.
1. Ngati mkadzi wanu akadali kugawa number yake mwachisawawa kwa amuna ena. Mlaliki 9:10.
2. Ngati mkadzi wanu akuvala zovala zoti Inu mkumulesa koma amavalira ndicholinga Choti amuna ena azimuona siwanu. 1 Peter 3:3.
3. Ngati mkadzi wanu akumalumikizanabe ndi ma ex Ake ziwani kuti mtima wake ukadali kuwakondabe amuna akale aja. Yesaya 43:18-19.-- mau amati zakale zapita....
4. Ngati mkadzi wanu samakupasani ulemu nthawi zonse amakhalira mwano, ndiye kuti alipo mwamuna amene amampasa ulemu. Efeso 5:33.
5. Ngati mkadzi wanu amagawana zinsinsi za mnyumba mwanu ndi amuna ena ziwani kuti mkadzi uyo siwanu. Mkadzi wanzeru amasunga zinsinsi za mnyumba mwanu. Miyambo 11:13.
- zikomo kwambiri mkhale ndi mmawa opambana nonse🥳🥳🥳🙏