25/09/2025
Pamene Mwakhalapo✍️ tiyeni tiphunzireko mu ka nkhani aka.
Mercy : hie bea
Gibo : hie honey
Mercy : boh
Gibo : bohboh
Mercy : ubwera lero?
Gibo : ayi ndipita kudimba
Mercy : chabwino! Koma dress lija wandigulira?
Gibo : ayi, udikire kaye ndipeze ganyu wowumba njerwa.
Mercy : chani? Mpaka kuwumba njerwa?
Gibo : eyaka, ndikakupasa ndalama ndimakhala ndagulitsa njerwa or foni ndidakugulira ija ndinkapelekera matope.
Mercy : iiiiii chabwino darling.
*After 3 months*
Mercy : hello my boy
Gibo : hello hun
Mercy : tikumane chonde
Gibo : ok chabwino
Mercy : kwathu andipatsa 200pin kuti ndikagule zovala koma ubwere udzatenge ndalamayi kuti uyambire
Ka business mwina upumeko
yowumba njerwayo.
Gibo : eeeeh ndalama yoseyo?
Mercy : eya dear dzatenge
Gibo : zikomo kwambiri my love
* After 6 months*
Makolo ake a Mercy adamwalira pa ngozi yagamoto, apa nkuti Gibo akupangabe business yake ndipo zinkamuyendera kwambiri
choncho adatenga udindo wolipira school fees ya Mercy mpaka kukoleji ndipo ankathandizaso abale ake a Mercy.
*Phunziro*
Amuna azanga tiyeni tizikhala a chikondi, okhulupilika komaso olimbikira pa njira yomwe imatipatsa ndalama.
Si akazi ose omwe amafuna ndalama, ena alipo amene amangofuna chikondi ndi kukhulupilika kwathu.
Choncho kudzichepetsa ndikwabwino osati kumana kuti mumagwira ntchito yapamwamba muzasemphana ndi madalitso.
Akazi inu, musamunyoze mwamuna chifukwa choti alibe ndalama moyowu ndiwozungulira sudziwa wodzakugwira nkono mawa lino chofunika ndichikondi chuma chimachita kubwera.
Anthu Ambiri Amadana ndi Mau A Mulungu Koma kukakhala Za dziko Monga Chuma ndi Zina zambiri amapanga follow komaso Cheya Koma Mau A Yehova Ayi😭 Ambuye ivani kulira
😭😭😭😭😭😭😭
Kwamwana wanu chonde mupatseni chomwe akufuna ngati akwanitse kulemba kuti Amen Ndikupanga follow 🤲🤲🙏🙏
Mukadina malemba awa 👉 Tilalike Uthenga ndikupanga follow komanso sheya Ngati ukuona post iyi
Zikomo powelenga ❤️