23/11/2024
Anthu muli busy kukamba zot akukuyu agendedwa koma simukuzuzura akachita aku L City ndiye kuyamba ku blema boma k*t likubweletsa nkhondo muno malawi ndiye akundilande sakubweletsa nkhodo komaso vuto lalikulu ndiinu apolice simukugwira ntchito yanu mwa u professionals tagwirani ntchito yanu mene munaphuzirira